Genesis 36:12 BL92

12 Ndipo Timna anali mkazi wace wamng'ono wa Elifazi mwana wamwamuna wa Esau; ndipo anambalira Elifazi Amaleki: amenewa ndi ana amuna a Ada mkazi wace wa Esau.

Werengani mutu wathunthu Genesis 36

Onani Genesis 36:12 nkhani