Genesis 36:43 BL92

43 mfumu Magidieli, mfumu Iramu; amenewa ndi mafumu a Edomu, monga mwa kukhala kwao m'dziko lokhala laolao. Uyo ndiye Esau atate wao wa Aedomu.

Werengani mutu wathunthu Genesis 36

Onani Genesis 36:43 nkhani