Genesis 37:35 BL92

35 Ndipo ana amuna ace onse ndi ana akazi onse anauka kuti amtonthoze: koma anakana kutonthozedwa; ndipo anati, Pakuti ndidzatsikira kumanda kwa mwana wanga, ndirinkulirabe. Atate wace ndipo anamlirira.

Werengani mutu wathunthu Genesis 37

Onani Genesis 37:35 nkhani