Genesis 4:14 BL92

14 Taonani, mwandiingitsa ine lero lomwe padziko; ndi pankhope panu ndidzabisika; ndipo ndidzakhala wothawathawa ndi woyendayenda pa dziko lapansi; ndipo kudzatero kuti onse akundipeza adzandipha.

Werengani mutu wathunthu Genesis 4

Onani Genesis 4:14 nkhani