Genesis 41:50 BL92

50 Ndipo kwa Yosefe anabadwa ana amuna awiri, cisanafike caka ca njala, amene Asenati mwana wamkazi wa Porifera wansembe wa Oni anambalira iye.

Werengani mutu wathunthu Genesis 41

Onani Genesis 41:50 nkhani