Genesis 42:38 BL92

38 Ndipo iye anati, Mwana wanga sadzatsikira ndi inu, cifukwa kuti mkuru wace wafa, ndipo watsala iye yekha; ngati coipa cikamgwera iye m'njira m'mene mupitamo, inu mudzatsitsira ndi cisoni imvi zanga kumanda.

Werengani mutu wathunthu Genesis 42

Onani Genesis 42:38 nkhani