Genesis 45:8 BL92

8 Ndipo tsopano sindinu amene munanditumiza ine ndifike kuno, koma Mulungu, ndipo anandiyesa ine atate wa Farao, ndi mwini banja lace lonse, ndi wolamulira dziko lonse la Aigupto.

Werengani mutu wathunthu Genesis 45

Onani Genesis 45:8 nkhani