Genesis 46:20 BL92

20 Kwa Yosefe kunabadwa m'dziko la Aigupto Manase ndi Efraimu, amene Asenati mwana wamkazi wa Potifera wansembe wa Oni anambalira iye.

Werengani mutu wathunthu Genesis 46

Onani Genesis 46:20 nkhani