Genesis 47:28 BL92

28 Ndipo Yakobo anakhala m'dziko la Aigupto zaka khumi mphambu zisanu ndi ziwiri; ndipo masiku a Yakobo zaka za moyo wace zinali zaka zana limodzi mphambu makumi anai kudza zisanu ndi ziwiri.

Werengani mutu wathunthu Genesis 47

Onani Genesis 47:28 nkhani