Genesis 47:30 BL92

30 koma pamene ndidzagona ndi makolo anga, udzanditenge ine kuturuka m'dziko la Aigupto, ukandiike ine m'manda mwao. Ndipo iye anati, Ndidzacita monga mwanena.

Werengani mutu wathunthu Genesis 47

Onani Genesis 47:30 nkhani