Genesis 48:19 BL92

19 Koma anakana atate wace, nati, Ndidziwa mwananga, ndidziwa; Iyenso adzakhala mtundu wa anthu, iyenso adzakula; koma mphwace adzakhala wamkuru ndi iye, ndipo mbeu zace zidzakhala mitundu yambirimbiri.

Werengani mutu wathunthu Genesis 48

Onani Genesis 48:19 nkhani