Genesis 50:11 BL92

11 Ndipo pamene anthu okhala m'dzikomo; Akanani, anaona maliro a m'dwale la Atadi, anati, Awa ndi maliro akuru a Aaigupto: cifukwa cace dzina la pamenepo linachedwa Abeli-mizraimu, pali tsidya lija la Yordano.

Werengani mutu wathunthu Genesis 50

Onani Genesis 50:11 nkhani