Genesis 6:3 BL92

3 Ndipo anati Yehova, Mzimu wanga sudzakangana ndi anthu nthawi zonse, cifukwa iwonso ndiwo thupi lanyama: koma masiku ace adzakhala zaka zana limodzi kudza makumi awiri.

Werengani mutu wathunthu Genesis 6

Onani Genesis 6:3 nkhani