Numeri 26:57 BL92

57 Ndipo awa ndi owerengedwa ao a Alevi monga mwa mabanja ao: Gerisoni, ndiye kholo la banja la Agerisoni; Kohati, ndiye kholo la banja la Akohati; Merari, ndiye kholo la banja la Amerari.

Werengani mutu wathunthu Numeri 26

Onani Numeri 26:57 nkhani