Numeri 26:65 BL92

65 Popeza Yehova adanena za iwowa, Adzafatu m'cipululu. Ndipo sanatsalira mmodzi wa iwowa koma Kalebi mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni.

Werengani mutu wathunthu Numeri 26

Onani Numeri 26:65 nkhani