Ezekieli 1:1 BL92

1 NDIPO kunali caka ca makumi atatu, mwezi wacinai, tsiku lacisanu la mwezi, pokhala ine pakati pa andende kumtsinje Kebara, kunatseguka kumwamba, ndipo ndinaona masomphenya a Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 1

Onani Ezekieli 1:1 nkhani