12 Ndipo thupi lao lonse, ndi misana yao, ndi manja ao, ndi mapiko ao, ndi njinga zomwe, zinadzala ndi maso pozungulira pao, zingakhale njingazi anai aja anali nazo.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 10
Onani Ezekieli 10:12 nkhani