Ezekieli 10:14 BL92

14 Ndipo ali yense anali nazo nkhope zinai, nkhope yoyamba ndiyo nkhope ya kerubi, ndi nkhope yaciwiri ndiyo nkhope ya munthu, ndi yacitatu ndiyo nkhope ya mkango, ndi yacinai ndiyo nkhope ya ciombankhanga.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 10

Onani Ezekieli 10:14 nkhani