Ezekieli 11:24 BL92

24 Ndipo mzimu unandikweza, nufika nane m'masomphenya mwa mzimu wa Mulungu ku dziko la Akasidi, kwa andendewo. M'mwemo masomphenya ndidawaona anandicokera, nakwera.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 11

Onani Ezekieli 11:24 nkhani