Ezekieli 12:7 BL92

7 Ndipo ndinacita monga momwe anandilamulira, ndinaturutsa akatundu anga usana, ngati a pa ulendo wa kundende, ndi madzulo ndinaboola pakhoma ndi dzanja langa, ndinawaturutsa pali mdima, ndi kuwasenza paphewa panga pamaso: pao.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 12

Onani Ezekieli 12:7 nkhani