Ezekieli 13:20 BL92

20 Cifukwa cace atero Ambuye Yehova, Taonani, nditsutsana nazo zophimbira zanu, zimene musaka nazo miyoyo komweko, kululuza; ndipo ndidzazikwatula m'manja mwanu, ndi kuimasula, ndiyo miyoyo muisaka kululuza.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 13

Onani Ezekieli 13:20 nkhani