Ezekieli 14:11 BL92

11 kuti nyumba ya Israyeli isasocerenso kusatsata Ine, kapena kudzidetsanso ndi zolakwa zao zonse; koma kuti akhale anthu anga, ndipo ndikhale Ine Mulungu wao, ati Ambuye Yehova.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 14

Onani Ezekieli 14:11 nkhani