18 cinkana anthu atatuwo akadakhala m'mwemo, Pali Ine, ati Ambuye Yehova, sakadapulumutsa ana amuna kapena akazi; koma iwo akadapulumuka okha.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 14
Onani Ezekieli 14:18 nkhani