9 Ndipo akaceteka mneneriyo, nakanena mau, Ine Yehova ndamceta mneneri uja; ndipo ndidzamtambasulira dzanja langa, ndi kumuononga pakati pa anthu anga Israyeli.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 14
Onani Ezekieli 14:9 nkhani