Ezekieli 16:27 BL92

27 Taona tsono, ndakutambasulira dzanja langa, ndi kucepsa gawo lako la cakudya, ndi kukupereka ku cifuniro ca iwo akudana nawe, kwa ana akazi a Afilisti akucita manyazi ndi njira yako yoipa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 16

Onani Ezekieli 16:27 nkhani