Ezekieli 16:33 BL92

33 Anthu amaninkha akazi onse acigololo mphatso, koma iwe umaninkha mabwenzi ako onse mphatso zako ndi kuwalipira, kuti akudzere kucokera ku mbali zonse, kuti acite nawe cigololo.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 16

Onani Ezekieli 16:33 nkhani