Ezekieli 17:24 BL92

24 Ndipo mitengo yonse ya kuthengo idzadziwa kuti Ine Yehova ndatsitsa mtengo wosomphoka, ndakuza mtengo waung'ono, ndaumitsa mtengo wauwisi, ndi kuphukitsa mtengo wouma; Ine Yehova ndanena ndi kucicita.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 17

Onani Ezekieli 17:24 nkhani