Ezekieli 18:17 BL92

17 naletsa dzanja lace pa wozunzika, wosalandira phindu kapena coonjezerapo, wocita maweruzo anga, nayenda m'malemba anga; uyu sadzafera mphulupulu ya atate wace, adzakhala ndi moyo ndithu.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 18

Onani Ezekieli 18:17 nkhani