19 Koma inu mukuti, Alekeranji mwana kusenza mphulupulu za atate wace? Mwanayo akacita ciweruzo ndi cilungamo, nakasunga malemba anga onse, ndi kuwacita, adzakhala ndi moyo ndithu.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 18
Onani Ezekieli 18:19 nkhani