Ezekieli 18:21 BL92

21 Koma woipayo akabwerera kusiya macimo ace onse adawacita nakasunga malemba anga onse, ndi kucita ciweruzo ndi cilungamo, adzakhala ndi moyo ndithu, sadzafa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 18

Onani Ezekieli 18:21 nkhani