Ezekieli 2:3 BL92

3 Nati kwa ine, Wobadwa ndi munthu iwe, ndikutumizira kwa ana a Israyeli, kwa mitundu ya anthu opanduka, amene anapandukana nane; iwo ndi makolo ao anandilakwira mpaka lero lomwe.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 2

Onani Ezekieli 2:3 nkhani