Ezekieli 2:8 BL92

8 Koma iwe, wobadwa ndi munthu, tamvera ici ndirikunena nawe; usakhale iwewopanduka, ngati nyumba ija yopanduka; tsegula pakamwa pako, nudye comwe ndikupatsa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 2

Onani Ezekieli 2:8 nkhani