Ezekieli 20:9 BL92

9 Koma ndinacicita cifukwa ca dzina langa, kuti lisadetsedwe pamaso pa amitundu amene anakhala pakati pao, amene pamaso pao ndinadzidziwitsa kwa iwo, pakuwaturutsa m'dziko la Aigupto.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 20

Onani Ezekieli 20:9 nkhani