Ezekieli 24:25 BL92

25 Ndipo wobadwa ndi munthu iwe, sikudzakhala kodi tsiku loti ndiwacotsera mphamvu yao, cimwemwe cao copambana, cowakonda m'maso mwao, ndi cokhumbitsa mtima wao, ana ao amuna ndi akazi,

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 24

Onani Ezekieli 24:25 nkhani