12 Ndipo adzalanda cuma cako ndi kufunkha malonda ako, nadzagwetsa malinga ako ndi kupasula nyumba zako zofunika, nadzaponya miyala yako, ndi mitengo yako, ndi pfumbi lako, m'madzi.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 26
Onani Ezekieli 26:12 nkhani