Ezekieli 26:2 BL92

2 Wobadwa ndi munthu iwe, popeza Turo ananyodola Yerusalemu, ndi kuti, Onyo, watyoka uwu udali cipata ca mitundu ya anthu; wanditembenukira ine; ndidzakhuta ine, wapasuka uwu;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 26

Onani Ezekieli 26:2 nkhani