Ezekieli 28:16 BL92

16 Mwa kucuruka kwa malonda ako anakudzaza m'kati mwako ndi ciwawa, ndipo unacimwa; cifukwa cace ndinakukankha kukucotsa pa phiri la Mulungu; ndipo ndinakuononga, kerubi wakuphimba iwe, kukucotsa pakati pa miyala yamoto.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 28

Onani Ezekieli 28:16 nkhani