Ezekieli 28:26 BL92

26 Nadzakhalamo osatekeseka, nadzamanga nyumba, ndi kunka mpesa m'mindamo, nadzakhalamo mosatekeseka, ndikatha kukwaniritsira maweruzo pa onse akuwapeputsa pozungulira pao; motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wao.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 28

Onani Ezekieli 28:26 nkhani