Ezekieli 29:12 BL92

12 Ndipo ndidzasandutsa dziko la Aigupto labwinja pakati pa maiko a mabwinja; ndi midzi yace pakati pa midzi yopasuka idzakhala yabwinja zaka makumi anai; ndipo ndidzamwaza Aaigupto mwa amitundu, ndi kuwabalalitsa m'maiko.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 29

Onani Ezekieli 29:12 nkhani