Ezekieli 29:3 BL92

3 nena, uziti, Atero Ambuye Yehova, Taona nditsutsana nawe, Farao mfumu ya Aigupto, ng'ona yaikuru yakugona m'kati mwa mitsinje yace, imene ikuti, Mtsinje wanga ndi wangatu, ndadzipangira ndekha uwu.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 29

Onani Ezekieli 29:3 nkhani