Ezekieli 30:18 BL92

18 Ndi ku Tehafinehesi kudzada usana, pakutyola Ine magoli a Aigupto komweko; ndi mphamvu yace yodzikuza idzalekeka m'menemo; kunena za ilo mtambo udzaliphimba, ndi ana ace akazi adzalowa undende.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 30

Onani Ezekieli 30:18 nkhani