Ezekieli 31:6 BL92

6 Mbalame zonse za m'mlengalenga zinamanga zisa zao pa nthambi zace, ndi pansi pa nthawi zace zinaswana nyama zonse za kuthengo, ndi pa mthunzi wace inakhala mitundu yonse yaikuru ya anthu.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 31

Onani Ezekieli 31:6 nkhani