Ezekieli 32:27 BL92

27 Koma sagona pamodzi ndi amphamvu osadulidwa adagwawo amene anatsikira kumanda ndi zida zao za nkhondo, amene anawatsamiritsa malupanga ao; ndi mphulupulu zao ziri pa mafupa ao; pakuti anaopsetsa amphamvu m'dziko la amoyo.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 32

Onani Ezekieli 32:27 nkhani