Ezekieli 33:13 BL92

13 Ndikanena kwa wolungama kuti adzakhala ndi moyo ndithu, akatama cilungamo cace, akacita cosalungama, sizikumbukika zolungama zace ziri zonse; koma m'cosalungama cace anacicita momwemo adzafa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 33

Onani Ezekieli 33:13 nkhani