Ezekieli 34:16 BL92

16 Ndidzafuna yotayika, ndi kubweza yopitikitsidwa, ndi kulukira chika yotyoka mwendo, ndi kulimbitsa yodwalayo; koma yanenepa ndi yolimba ndidzaziononga, ndidzazidyetsa ndi ciweruzo.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 34

Onani Ezekieli 34:16 nkhani