Ezekieli 36:3 BL92

3 cifukwa cace unenere, nuti, Atero Ambuye Yehova, Cifukwa, inde cifukwa kuti anakupasulani, nakumemezani pozungulira ponse, kuti mukhale colowa ca amitundu otsala, ndipo mwafika pa milomo ya akazitape, ndi pa mbiri yoipa ya anthu;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 36

Onani Ezekieli 36:3 nkhani