Ezekieli 36:6 BL92

6 Cifukwa cace unenere za dziko la Israyeli, nuti kwa mapiri ndi kwa zitunda, kwa mitsinje ndi kwa zigwa, Atero Ambuye Yehova, Taonani, ndalankhula mu nsanje yanga ndi ukali wanga, popeza mwasenza manyazi a amitundu;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 36

Onani Ezekieli 36:6 nkhani