Ezekieli 37:22 BL92

22 ndipo ndidzawayesa mtundu umodzi m'dzikomo, pa mapiri a Israyeli; ndipo mfumu imodzi idzakhala mfumu ya iwo onse, sadzakhalanso mitundu iwiri, kapena kugawanikanso maufumu awiri konse ai.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 37

Onani Ezekieli 37:22 nkhani