Ezekieli 39:23 BL92

23 Ndipo amitundu adzadziwa kuti nyumba ya Israyeli idalowa undende cifukwa ca mphulupulu zao, popeza anandilakwira Ine; ndipo ndinawabisira nkhope yanga; m'mwemo ndinawapereka m'dzanja la adani ao, nagwa iwo onse ndi lupanga.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 39

Onani Ezekieli 39:23 nkhani