Ezekieli 40:12 BL92

12 ndi pakhomo pa zipinda za alonda panali kakhoma ka mkono umodzi cakuno, ndi kakhoma ka mkono umodzi cauko; ndi zipinda za alonda mikono isanu ndi umodzi cakuno, ndi mikono isanu ndi umodzi cauko.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 40

Onani Ezekieli 40:12 nkhani